[Verse 1: Praise Umali]
I worried all the time
I thought I'm running out of time
Can't take it a day at a time sometimes
Man our dreams have been too loud since
We were only young kids
And now, we grown they loud still
I know ndizambiri umafuna mtima
Nde pena mantha ankadzandigwila
Like what if we don't make it (yeah yeah)
What if we don't make it (yeah yeah)
[Chorus: Praise Umali]
Koma tachoka nkutali
Mulungu anali ndi pulani
Pulani
Inu Zonse ndi nthawi
Mulungu anali ndi pulani
Pulani
Yopanga za ifeyo (oooh oooh oooh)
Yopanga za ifeyo
Akupanga za ifeyo (oooh oooh oooh)
Akupanga za ifeyo
[Verse 2: Gwamba]
Yoh
Venue yomweyo ena amaflopa
Samatrenda nyimbo zawo akadropa
Nde pena pride imafuna idzindikopa
Koma mbuye wanga sangakondwe kuti nzizipopa
Nde rule number 1, kumakhala humble
Poti ukazikweza amasiya kupanga zako
Rule number 2, osakhala ndi tsankho
Poti lero ndi kape mawa ali pamwamba pako
Nkayang'ana kumbuyo ngati ndingokuwa mbuye
Ndinakhonza chani kuti inu mundimasule
Mwandichotsa kutali kwinakunso Mulambule
Ulendowu ndiwautali koma
[Chorus: Praise Umali]
Koma tachoka nkutali
Mulungu anali ndi pulani
Pulani
Inu Zonse ndi nthawi
Mulungu anali ndi pulani
Pulani
Yopanga za ifeyo (oooh oooh oooh)
Yopanga za ifeyo
Akupanga za ifeyo (oooh oooh oooh)
Akupanga za ifeyo
Plan was written by Praise Umali & Gwamba.
Plan was produced by Praise Umali.
Praise Umali released Plan on Sat Sep 24 2022.